1
Gen. 29:20
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Motero Yakobe adagwira ntchito zaka zisanu ndi ziŵiri kuti akwatire Rakele, ndipo nthaŵi imeneyo idangooneka kwa iye ngati masiku oŵerengeka chabe, chifukwa choti adaamkonda kwambiri mkaziyo.
Compare
Explore Gen. 29:20
2
Gen. 29:31
Chauta ataona kuti Yakobe sankakonda kwambiri Leya, adalola kuti Leyayo abale ana, koma Rakele ai.
Explore Gen. 29:31