1
AROMA 15:13
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Mulungu wa chiyembekezo adzaze inu ndi chimwemwe chonse ndi mtendere m'kukhulupirira, kuti mukachuluke ndi chiyembekezo, mu mphamvu ya Mzimu Woyera.
Compare
Explore AROMA 15:13
2
AROMA 15:4
Pakuti zonse zinalembedwa kale zinalembedwa kutilangiza, kuti mwa chipiriro ndi chitonthozo cha malembo, tikhale ndi chiyembekezo.
Explore AROMA 15:4
3
AROMA 15:5-6
Ndipo Mulungu wa chipiriro ndi wa chitonthozo apatse inu kuti mukhale ndi mtima umodzi wina ndi mnzake, monga mwa Khristu Yesu; kuti nonse pamodzi, m'kamwa mmodzi, mukalemekeze Mulungu ndi Atate wa Ambuye wathu Yesu Khristu.
Explore AROMA 15:5-6
4
AROMA 15:7
Chifukwa chake mulandirane wina ndi mnzake, monganso Khristu anakulandirani inu, kukachitira Mulungu ulemerero.
Explore AROMA 15:7
5
AROMA 15:2
Yense wa ife akondweretse mnzake, kumchitira zabwino, zakumlimbikitsa.
Explore AROMA 15:2
Home
Bible
Plans
Videos