1
LEVITIKO 26:12
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo ndidzayendayenda pakati pa inu, ndi kukhala Mulungu wanu ndi inu mudzakhala anthu anga.
Compare
Explore LEVITIKO 26:12
2
LEVITIKO 26:4
ndidzakupatsani mvula m'nyengo zake, ndi dziko lidzapereka zipatso zake, ndi mitengo ya m'minda idzabala zipatso zake.
Explore LEVITIKO 26:4
3
LEVITIKO 26:3
Mukamayenda m'malemba anga, ndi kusunga malamulo anga, ndi kuwachita
Explore LEVITIKO 26:3
4
LEVITIKO 26:6
Ndipo ndidzapatsa mtendere m'dzikomo, kuti mudzagone pansi, wopanda wina wakukuopsani; ndidzaletsanso zilombo zisakhale m'dzikomo, lupanga lomwe silidzapita m'dziko mwanu.
Explore LEVITIKO 26:6
5
LEVITIKO 26:9
Ndipo ndidzatembenukira kwa inu, ndi kukubalitsani, ndi kukuchulukitsani; ndipo ndidzakhazika chipangano changa ndinapangana nanucho.
Explore LEVITIKO 26:9
6
LEVITIKO 26:13
Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndinakutulutsani m'dziko la Ejipito, kuti musakhale akapolo ao; ndipo ndinathyola mitengo ya magoli anu, ndi kukuyendetsani choweramuka.
Explore LEVITIKO 26:13
7
LEVITIKO 26:11
Ndidzamanga Kachisi wanga pakati pa inu, ndipo moyo wanga sudzanyansidwa nanu.
Explore LEVITIKO 26:11
8
LEVITIKO 26:1
Musamadzipangira mafano, kapena kudziutsira mafano osema, kapena choimiritsa, kapena kuika mwala wozokota m'dziko mwanu kuugwadira umene; popeza Ine ndine Yehova Mulungu wanu.
Explore LEVITIKO 26:1
9
LEVITIKO 26:10
Ndipo mudzadya za sundwe wakale ndi kutulutsa zakale chifukwa cha zatsopano.
Explore LEVITIKO 26:10
10
LEVITIKO 26:8
Asanu a inu adzapirikitsa zana limodzi, ndi zana limodzi la inu adzapirikitsa zikwi khumi; ndi adani anu adzagwa pamaso panu ndi lupanga.
Explore LEVITIKO 26:8
11
LEVITIKO 26:5
Ndipo nyengo yopuntha tirigu idzafikira nyengo yotchera mphesa, ndi nyengo yotchera mphesa idzafikira nyengo zobzala; ndipo mudzakhuta nacho chakudya chanu, ndi kukhala m'dziko mwanu okhazikika.
Explore LEVITIKO 26:5
12
LEVITIKO 26:7
Mudzapirikitsa adani anu, ndipo adzagwa pamaso panu ndi lupanga.
Explore LEVITIKO 26:7
13
LEVITIKO 26:2
Musunge masabata anga, ndi kuchitira ulemu malo anga opatulika; Ine ndine Yehova.
Explore LEVITIKO 26:2
Home
Bible
Plans
Videos