1
YOSWA 21:45
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Sikadasowa kanthu konse ka zinthu zokoma zonse Yehova adazinenera nyumba ya Israele; zidachitika zonse.
Compare
Explore YOSWA 21:45
2
YOSWA 21:44
Ndipo Yehova anawapatsa mpumulo pozungulira ponse, monga mwa zonse adalumbirira makolo ao; ndipo pamaso pao sipanaima munthu mmodzi wa adani ao onse; Yehova anapereka adani ao onse m'manja mwao.
Explore YOSWA 21:44
3
YOSWA 21:43
Motero Yehova anawapatsa Israele dziko lonse adalumbiralo kuwapatsa makolo ao: ndipo analilandira laolao, nakhala m'mwemo.
Explore YOSWA 21:43
Home
Bible
Plans
Videos