1
YESAYA 37:16
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele, amene mukhala pa akerubi, Inu ndinu Mulungu, Inu nokha, wa maufumu onse a dziko lapansi, Inu munalenga kumwamba ndi dziko lapansi.
Compare
Explore YESAYA 37:16
2
YESAYA 37:20
Chifukwa chake, Yehova, Mulungu wathu, mutipulumutse ife m'manja mwake, kuti maufumu onse a dziko adziwe, kuti Inu ndinu Yehova, Inu nokha.
Explore YESAYA 37:20