1
YESAYA 32:17
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndi ntchito ya chilungamo idzakhala mtendere; ndi zotsata chilungamo zidzakhala mtendere, ndi kukhulupirika kunthawi zonse.
Compare
Explore YESAYA 32:17
2
YESAYA 32:18
Ndipo anthu anga adzakhala m'malo a mtendere, ndi mokhala mokhulupirika ndi mopuma mwa phee.
Explore YESAYA 32:18