1
HABAKUKU 1:5
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Penyani mwa amitundu, penyetsetsani, nimudabwe kwakukulu, pakuti ndichita ntchito masiku anu, imene simudzavomera chinkana akufotokozerani.
Compare
Explore HABAKUKU 1:5
2
HABAKUKU 1:2
Yehova, ndidzafuula mpaka liti osamva Inu? Ndifuulira kwa Inu za chiwawa, koma simupulumutsa.
Explore HABAKUKU 1:2
3
HABAKUKU 1:3
Mundionetseranji zopanda pake, ndi kundionetsa zovuta? Pakuti kufunkha ndi chiwawa zili pamaso panga; ndipo pali ndeu, nauka makani.
Explore HABAKUKU 1:3
4
HABAKUKU 1:4
Pakuti chilamulo chalekeka, ndi chiweruzo sichitulukira konse; popeza woipa azinga wolungama, chifukwa chake chiweruzo chituluka chopindika.
Explore HABAKUKU 1:4
Home
Bible
Plans
Videos