1
EKSODO 28:3
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo ulankhule ndi onse a mtima waluso, amene ndawadzaza ndi mzimu waluso, kuti amsokere Aroni zovala apatulidwe nazo, andichitire Ine ntchito ya nsembe.
Compare
Explore EKSODO 28:3
2
EKSODO 28:4
Ndipo zovala azisoka ndizi: chapachifuwa ndi efodi, ndi mwinjiro, ndi malaya opikapika, ndi nduwira, ndi mpango; tero apangire Aroni mbale wako ndi ana ake zovala zopatulika, kuti andichitire Ine ntchito ya nsembe.
Explore EKSODO 28:4
Home
Bible
Plans
Videos