1
Zekariya 7:9
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Muziweruza molungama; muzichitirana chifundo ndi kumverana chisoni.
Compare
Explore Zekariya 7:9
2
Zekariya 7:10
Musamazunze akazi amasiye kapena ana amasiye, alendo kapena osauka. Musamaganizirane zoyipa mʼmitima mwanu.’
Explore Zekariya 7:10