1
Afilipi 4:6
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Musade nkhawa ndi kanthu kalikonse, koma pa china chilichonse, mwa pemphero ndi chidandaulo pamodzi ndi chiyamiko, perekani zopempha zanu kwa Mulungu.
Compare
Explore Afilipi 4:6
2
Afilipi 4:7
Ndipo mtendere wa Mulungu, umene upambana nzeru zonse udzasunga bwino mitima yanu ndi maganizo anu mwa Khristu Yesu.
Explore Afilipi 4:7
3
Afilipi 4:8
Potsiriza, abale, muziyika mtima wanu pa zinthu zilizonse zabwino ndi zotamandika monga, zinthu zoona, zinthu zolemekezeka, zinthu zolungama, zinthu zoyera, zinthu zokongola ndi zinthu zosiririka.
Explore Afilipi 4:8
4
Afilipi 4:13
Ndikhoza kuchita zonse kudzera mwa Iye amene amandipatsa mphamvu.
Explore Afilipi 4:13
5
Afilipi 4:4
Nthawi zonse muzikondwa mwa Ambuye. Ndikubwerezanso; muzikondwa!
Explore Afilipi 4:4
6
Afilipi 4:19
Ndipo Mulungu wanga adzakwaniritsa zosowa zanu monga mwa chuma chake chaulemerero mwa Khristu Yesu.
Explore Afilipi 4:19
7
Afilipi 4:9
Muzichita chilichonse chimene mwaphunzira kapena kulandira kapena kumva kuchokera kwa ine kapena mwaona mwa ine. Ndipo Mulungu wamtendere adzakhala nanu.
Explore Afilipi 4:9
8
Afilipi 4:5
Kufatsa kwanu kuzioneka pamaso pa anthu onse. Ambuye anu ali pafupi.
Explore Afilipi 4:5
9
Afilipi 4:12
Ndimadziwa kusauka nʼkutani, ndipo ndimadziwa kulemera nʼkutani. Ndaphunzira chinsinsi chokhala wokhutitsidwa mwa njira ina iliyonse, kaya nʼkudya bwino kapena kukhala ndi njala, kaya kukhala ndi chuma kapena umphawi.
Explore Afilipi 4:12
10
Afilipi 4:11
Sindikunena izi chifukwa choti ndikusowa thandizo, poti ine ndaphunzira kukhala wokwaniritsidwa ndi zimene ndili nazo.
Explore Afilipi 4:11
Home
Bible
Plans
Videos