1
Numeri 23:19
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Mulungu si munthu kuti aname, kapena mwana wa munthu kuti asinthe maganizo ake. Kodi amayankhula koma osachita? Kodi amalonjeza koma osakwaniritsa?
Compare
Explore Numeri 23:19
2
Numeri 23:23
Palibe matsenga amene angalimbane ndi Yakobo, palibe mawula amene angalimbane ndi Israeli. Tsopano za Yakobo ndi Israeli adzanena kuti, ‘Onani zimene Mulungu wachita!’
Explore Numeri 23:23
3
Numeri 23:20
Wandilamula kuti ndidalitse, Iyeyo wadalitsa ndipo sindingasinthe.
Explore Numeri 23:20