1
Numeri 17:8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Pa tsiku lotsatira Mose analowa mu tenti ya msonkhanoyo ndipo anaona kuti ndodo ya Aaroni, yomwe inkayimira fuko la Levi, sinangophuka masamba chabe, komanso inachita maluwa nʼkubala zipatso za alimondi.
Compare
Explore Numeri 17:8