1
Yeremiya 10:23
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Inu Yehova, ndikudziwa kuti moyo umene munthu ali nawo si wake; munthuyo sangathe kuwongolera mayendedwe ake.
Compare
Explore Yeremiya 10:23
2
Yeremiya 10:6
Palibe wofanana nanu, Inu Yehova; Inu ndinu wamkulu, ndipo dzina lanu lili ndi mphamvu yayikulu.
Explore Yeremiya 10:6
3
Yeremiya 10:10
Koma Yehova ndiye Mulungu woona; Iyeyo ndiye Mulungu wamoyo, Mfumu yamuyaya. Akakwiya, dziko limagwedezeka; anthu a mitundu ina sangathe kupirira ukali wakewo.
Explore Yeremiya 10:10
4
Yeremiya 10:24
Inu Yehova, langizeni, komatu mwachilungamo, osati ndi mkwiyo wanu, mungandiwononge kotheratu.
Explore Yeremiya 10:24