1
Yeremiya 1:5
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
“Ndisanakuwumbe mʼmimba mwa amayi ako ndinali nditakudziwa kale, iwe usanabadwe ndinali nditakupatula kale; ndinakuyika kuti ukhale mneneri kwa anthu a mitundu yonse.”
Compare
Explore Yeremiya 1:5
2
Yeremiya 1:8
Usawaope, pakuti Ine ndili nawe, ndipo ndidzakupulumutsa,” akutero Yehova.
Explore Yeremiya 1:8
3
Yeremiya 1:19
Iwo adzalimbana nawe koma sadzakugonjetsa, popeza Ine ndili nawe ndipo ndidzakupulumutsa,” akutero Yehova.
Explore Yeremiya 1:19