1
Yesaya 5:20
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Tsoka kwa amene zoyipa amaziyesa zabwino ndipo zabwino amaziyesa zoyipa, amene mdima amawuyesa kuwala ndipo kuwala amakuyesa mdima, amene zowawasa amaziyesa zotsekemera ndipo zotsekemera amaziyesa zowawasa.
Compare
Explore Yesaya 5:20
2
Yesaya 5:21
Tsoka kwa amene amadziona ngati anzeru ndipo amadziyesa ochenjera.
Explore Yesaya 5:21
3
Yesaya 5:13
Motero anthu anga adzatengedwa ukapolo chifukwa cha kusamvetsa zinthu; atsogoleri awo olemekezeka adzafa ndi njala, ndipo anthu wamba ochuluka adzafa ndi ludzu.
Explore Yesaya 5:13