1
Yesaya 3:10
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Nena kwa olungama kuti zonse zidzawayendera bwino, pakuti adzakondwera ndi phindu la ntchito zawo.
Compare
Explore Yesaya 3:10
2
Yesaya 3:11
Tsoka kwa anthu oyipa! Mavuto ali pa iwo! Adzalandira malipiro a zimene manja awo anachita.
Explore Yesaya 3:11