1
Yesaya 22:22
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ndidzamupatsa ulamuliro wa banja la Davide. Adzatsekula ndipo palibe adzatseke, adzatseka popanda wina kutsekula.
Compare
Explore Yesaya 22:22
2
Yesaya 22:23
Ufumu wake udzakhala wokhazikika ngati chikhomo chokhomedwa pa malo olimba. Anthu adzalemekeza nyumba ya abale ake chifukwa cha iye.
Explore Yesaya 22:23