1
Yesaya 17:1
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Uthenga wonena za Damasiko: “Taonani, mzinda wa Damasiko sudzakhalanso mzinda, koma udzasanduka bwinja.
Compare
Explore Yesaya 17:1
2
Yesaya 17:3
Ku Efereimu sikudzakhalanso linga, ndipo ku Damasiko sikudzakhalanso ufumu; Otsalira a ku Siriya adzachotsedwa ulemu monga anthu a ku Israeli,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Explore Yesaya 17:3
3
Yesaya 17:4
“Tsiku limenelo ulemerero wa Yakobo udzazimirira; ndipo chuma chake chidzasanduka umphawi.
Explore Yesaya 17:4
4
Yesaya 17:2
Mizinda ya Aroeri idzakhala yopanda anthu ndipo idzakhala ya ziweto, zimene zidzagona pansi popanda wina woziopseza.
Explore Yesaya 17:2