1
Hoseya 11:4
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ndinawatsogolera ndi zingwe zachifundo cha anthu ndi zomangira za chikondi; ndinachotsa goli mʼkhosi mwawo ndipo ndinawerama nʼkuwadyetsa.
Compare
Explore Hoseya 11:4
2
Hoseya 11:1
“Israeli ali mwana, ndinamukonda, ndipo ndinayitana mwana wanga kuti atuluke mu Igupto.
Explore Hoseya 11:1