1
Eksodo 39:43
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Mose anayendera ntchitoyo ndipo anaona kuti anayichita monga momwe Yehova analamulira. Kotero Mose anawadalitsa.
Compare
Explore Eksodo 39:43
2
Eksodo 39:42
Aisraeli anagwira ntchito yonse monga momwe Yehova analamulira Mose.
Explore Eksodo 39:42
3
Eksodo 39:32
Tsopano ntchito yonse ya tenti ya msonkhano inatha. Aisraeli anachita zonse monga momwe Yehova analamulira Mose.
Explore Eksodo 39:32