1
Eksodo 14:14
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Yehova adzakumenyerani nkhondo. Inu mungokhala chete.”
Compare
Explore Eksodo 14:14
2
Eksodo 14:13
Mose anayankha anthu kuti, “Musachite mantha. Imani, ndipo muone chipulumutso chimene Yehova akuchitireni lero. Aigupto amene mukuwaona lerowa simudzawaonanso.
Explore Eksodo 14:13
3
Eksodo 14:16
Nyamula ndodo yako ndi kutambasula dzanja lako kuloza ku nyanja, kugawa madzi kuti Aisraeli awoloke powuma.
Explore Eksodo 14:16
4
Eksodo 14:31
Choncho Aisraeli anaona dzanja lamphamvu la Yehova limene linagonjetsa Aigupto aja, ndipo iwo anaopa Yehova ndi kumukhulupirira pamodzi ndi mtumiki wake Mose.
Explore Eksodo 14:31