Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

MARKO 4:39-40

MARKO 4:39-40 BLPB2014

Ndipo anauka, nadzudzula mphepo, nati kwa nyanja, kuti, Tonthola, khala bata. Ndipo mphepo inaleka, ndipo kunagwa bata lalikulu. Ndipo ananena nao, Muchitiranji mantha? Kufikira tsopano mulibe chikhulupiriro kodi?

Video zinazohusiana

Mipango ya Kusoma Bila Malipo na Ibada zinazohusiana na MARKO 4:39-40