Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

MATEYU 7:15-16

MATEYU 7:15-16 BLPB2014

Yang'anirani mupewe aneneri onyenga, amene adza kwa inu ndi zovala zankhosa, koma m'kati mwao ali mimbulu yolusa. Mudzawazindikira ndi zipatso zao. Kodi atchera mphesa paminga, kapena nkhuyu pamtula?