Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

MATEYU 5:15-16

MATEYU 5:15-16 BLPB2014

Kapena sayatsa nyali, ndi kuivundikira m'mbiya, koma aiika iyo pa choikapo chake; ndipo iunikira onse ali m'nyumbamo. Chomwecho muwalitse inu kuunika kwanu pamaso pa anthu, kuti pakuona ntchito zanu zabwino, alemekeze Atate wanu wa Kumwamba.

Mipango ya Kusoma Bila Malipo na Ibada zinazohusiana na MATEYU 5:15-16