1
ZEFANIYA 3:17
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Yehova Mulungu wako ali pakati pako, wamphamvu wakupulumutsa; adzakondwera nawe ndi chimwemwe, adzakhala wopanda thamo m'chikondi chake; adzasekerera nawe ndi kuimbirapo.
Linganisha
Chunguza ZEFANIYA 3:17
2
ZEFANIYA 3:20
Nthawi yomweyo ndidzakulowetsani, ndi nthawi yomweyo ndidzakusonkhanitsani; pakuti ndidzakuikani mukhale dzina, ndi chilemekezo mwa mitundu yonse ya anthu a pa dziko lapansi, pamene ndibweza undende wanu pamaso panu, ati Yehova.
Chunguza ZEFANIYA 3:20
3
ZEFANIYA 3:15
Yehova wachotsa maweruzo ako, anataya kunja mdani wako; mfumu ya Israele, Yehova, ali pakati pako, sudzaopanso choipa.
Chunguza ZEFANIYA 3:15
4
ZEFANIYA 3:19
Taonani, nthawi yomweyo ndidzachita nao onse akuzunza iwe; ndipo ndidzapulumutsa wotsimphinayo, ndi kusonkhanitsa wopirikitsidwayo; ndipo ndidzawaika akhale chilemekezo ndi dzina, iwo amene manyazi ao anali m'dziko lonse.
Chunguza ZEFANIYA 3:19
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video