Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

ZEFANIYA 3:20

ZEFANIYA 3:20 BLPB2014

Nthawi yomweyo ndidzakulowetsani, ndi nthawi yomweyo ndidzakusonkhanitsani; pakuti ndidzakuikani mukhale dzina, ndi chilemekezo mwa mitundu yonse ya anthu a pa dziko lapansi, pamene ndibweza undende wanu pamaso panu, ati Yehova.