1
ZEKARIYA 10:1
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pemphani kwa Yehova mvula, m'nyengo ya mvula ya masika, kwa Yehova wolenga mphezi; ndipo adzawapatsa mivumbi ya mvula, kwa yense zophukira kuthengo.
Linganisha
Chunguza ZEKARIYA 10:1
2
ZEKARIYA 10:12
Ndipo ndidzawalimbitsa mwa Yehova; ndipo adzayendayenda m'dzina lake; ati Yehova.
Chunguza ZEKARIYA 10:12
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video