1
AROMA 15:13
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Mulungu wa chiyembekezo adzaze inu ndi chimwemwe chonse ndi mtendere m'kukhulupirira, kuti mukachuluke ndi chiyembekezo, mu mphamvu ya Mzimu Woyera.
Linganisha
Chunguza AROMA 15:13
2
AROMA 15:4
Pakuti zonse zinalembedwa kale zinalembedwa kutilangiza, kuti mwa chipiriro ndi chitonthozo cha malembo, tikhale ndi chiyembekezo.
Chunguza AROMA 15:4
3
AROMA 15:5-6
Ndipo Mulungu wa chipiriro ndi wa chitonthozo apatse inu kuti mukhale ndi mtima umodzi wina ndi mnzake, monga mwa Khristu Yesu; kuti nonse pamodzi, m'kamwa mmodzi, mukalemekeze Mulungu ndi Atate wa Ambuye wathu Yesu Khristu.
Chunguza AROMA 15:5-6
4
AROMA 15:7
Chifukwa chake mulandirane wina ndi mnzake, monganso Khristu anakulandirani inu, kukachitira Mulungu ulemerero.
Chunguza AROMA 15:7
5
AROMA 15:2
Yense wa ife akondweretse mnzake, kumchitira zabwino, zakumlimbikitsa.
Chunguza AROMA 15:2
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video