Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

AROMA 15:5-6

AROMA 15:5-6 BLPB2014

Ndipo Mulungu wa chipiriro ndi wa chitonthozo apatse inu kuti mukhale ndi mtima umodzi wina ndi mnzake, monga mwa Khristu Yesu; kuti nonse pamodzi, m'kamwa mmodzi, mukalemekeze Mulungu ndi Atate wa Ambuye wathu Yesu Khristu.

Video ya AROMA 15:5-6