1
LUKA 10:19
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Taonani, ndakupatsani ulamuliro wakuponda pa njoka ndi zinkhanira, ndi pa mphamvu iliyonse ya mdaniyo; ndipo kulibe kanthu kadzakuipsani konse.
Linganisha
Chunguza LUKA 10:19
2
LUKA 10:41-42
Koma Ambuye anayankha nati kwa iye, Marita, Marita, uda nkhawa nuvutika ndi zinthu zambiri; koma chisoweka chinthu chimodzi, pakuti Maria anasankha dera lokoma limene silidzachotsedwa kwa iye.
Chunguza LUKA 10:41-42
3
LUKA 10:27
Ndipo iye anayankha nati, Uzikonda Ambuye Mulungu wako ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi mphamvu yako yonse, ndi nzeru zako zonse, ndi mnansi wako monga iwe mwini.
Chunguza LUKA 10:27
4
LUKA 10:2
Ndipo ananena kwa iwo, Dzinthu dzichuluka, koma antchito achepa; potero pemphani Mwini dzinthu, kuti akankhe antchito kukututa kwake.
Chunguza LUKA 10:2
5
LUKA 10:36-37
Uti wa awa atatu, uyesa iwe, anakhala mnansi wa iye uja adagwa m'manja a achifwamba? Ndipo anati, Iye wakumchitira chifundo. Ndipo Yesu anati kwa iye, Pita nuchite iwe momwemo.
Chunguza LUKA 10:36-37
6
LUKA 10:3
Mukani; taonani, Ine ndituma inu ngati anaankhosa pakati pa mimbulu.
Chunguza LUKA 10:3
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video