Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

LUKA 10:41-42

LUKA 10:41-42 BLPB2014

Koma Ambuye anayankha nati kwa iye, Marita, Marita, uda nkhawa nuvutika ndi zinthu zambiri; koma chisoweka chinthu chimodzi, pakuti Maria anasankha dera lokoma limene silidzachotsedwa kwa iye.

Mipango ya Kusoma Bila Malipo na Ibada zinazohusiana na LUKA 10:41-42