1
2 AKORINTO 11:14-15
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo kulibe kudabwa; pakuti Satana yemwe adzionetsa ngati mngelo wa kuunika. Chifukwa chake sikuli kanthu kwakukulu ngatinso atumiki ake adzionetsa monga atumiki a chilungamo; amene chimaliziro chao chidzakhala monga ntchito zao.
Linganisha
Chunguza 2 AKORINTO 11:14-15
2
2 AKORINTO 11:3
Koma ndiopa, kuti pena, monga njoka inanyenga Heva ndi kuchenjerera kwake, maganizo anu angaipsidwe kusiyana nako kuona mtima ndi kuyera mtima zili kwa Khristu.
Chunguza 2 AKORINTO 11:3
3
2 AKORINTO 11:30
Ngati ndiyenera kudzitamandira, ndidzadzitamandira ndi za kufooka kwanga.
Chunguza 2 AKORINTO 11:30
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video