YouVersion logga
BibelnLäsplanerVideor
Skaffa appen
Språkväljare
Sök ikon

Populära bibelverser från Genesis 2

1

Genesis 2:24

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Nʼchifukwa chake, mwamuna amasiya abambo ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake ndipo awiriwo amakhala thupi limodzi.

Jämför

Utforska Genesis 2:24

2

Genesis 2:18

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Yehova Mulungu anati, “Sibwino kuti munthu akhale yekha. Ndidzamupangira mnzake womuthandiza.”

Jämför

Utforska Genesis 2:18

3

Genesis 2:7

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Tsono Yehova Mulungu anawumba munthu kuchokera ku dothi nawuziramo mpweya wamoyo mʼmphuno mwake ndipo munthuyo anakhala wamoyo.

Jämför

Utforska Genesis 2:7

4

Genesis 2:23

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Munthu uja anati, “Uyu ndiye fupa lochokera ku mafupa anga ndi mnofu wochokera ku mnofu wanga; adzatchedwa ‘mkazi,’ popeza wachokera mwa mwamuna.”

Jämför

Utforska Genesis 2:23

5

Genesis 2:3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Mulungu anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri nalipatula, chifukwa pa tsiku limeneli Iye anapumula ku ntchito yonse yolenga imene anayigwira.

Jämför

Utforska Genesis 2:3

6

Genesis 2:25

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Munthu uja ndi mkazi wakeyo, onse awiri anali maliseche ndipo analibe manyazi.

Jämför

Utforska Genesis 2:25

Föregående kapitel
Nästa kapitel
YouVersion

Uppmuntrar och utmanar dig att söka Guds närhet varje dag.

Tjänst

Om

Karriärer

Volontär

Blogg

Press

Användbara länkar

Hjälp

Donera

Bibelöversättningar

Ljudbiblar

Bibelspråk

Dagens vers


En digital tjänst från

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

IntegritetspolicyVillkor
Åtgärdsprogram för säkerhet
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Hem

Bibeln

Läsplaner

Videor