1
Matayo 14:30-31
Nyanja
NTNYBL2025
Petulo yapo wadawona mbhepo yaikulu, wadaopa ni kuyamba kubila uku niwabula phokoso, “Ambuye, nipulumucheni!” Pampajha, Yesu wadatambasula jhanja lake, wadamgwila ni kumkambila, “Iwe wa chikulupi chochepa, ndande yanji uopa?”
Comparar
Explorar Matayo 14:30-31
2
Matayo 14:30
Petulo yapo wadawona mbhepo yaikulu, wadaopa ni kuyamba kubila uku niwabula phokoso, “Ambuye, nipulumucheni!”
Explorar Matayo 14:30
3
Matayo 14:27
Nambho pampajha Yesu wadaakambila, “Jhithileni mtima, ni ine. Msadaopa!”
Explorar Matayo 14:27
4
Matayo 14:28-29
Petulo wadamkambila, “Ambuye, ngati nde imwe, nikambileni nikuchateni pakuyenda pa mwamba pa majhi.” Yesu wadamkambila, “Chabwino, majha.” Ndiipo Petulo wadachika mbwato waukulu, wadayenda pamwamba pa majhi ni kumpitila Yesu.
Explorar Matayo 14:28-29
5
Matayo 14:33
Wonjhe adali mbwato waukulu, adagwada ni kumkwatamila, niakamba, “Zenedi iwe ni Mwana wa Mnungu.”
Explorar Matayo 14:33
6
Matayo 14:16-17
Yesu wadaakambila, “Siifunika achoke, anyiimwe mwachinawene wake mwaapache chakudya.” Anyiiwo adamuyangha, “Tulinayo mabumunda isanope ni njhomba ziwili.”
Explorar Matayo 14:16-17
7
Matayo 14:18-19
Yesu wadaakambila, “Nipelekeleni pano.” Wadaakambila wandhu akhale mmaujhu. Yesu wadatenga mabumunda yasano ni njhombha ziwili zijha, wadakweza maso yake kumwamba, wadamyamika Mnungu. Halafu wadabandhula mabumunda ni kwaapacha oyaluzidwa wake, naonjho oyaluzidwa wake wadaagawila wandhu.
Explorar Matayo 14:18-19
8
Matayo 14:20
Wandhu wonjhe adadya ni kukhuta. Oyaluzidwa adakokola vidufya ivo vidakhalila ni kujhaza miseche khumi ni iwili.
Explorar Matayo 14:20
Inicio
Biblia
Planes
Vídeos