Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

Matayo 24:9-11

Matayo 24:9-11 NTNYBL2025

“Ndiipo sakugwileni kuti mvutichidwe ni kuphedwa. Wandhu a maiko yonjhe siyakuipileni ndande anyiimwe ni oyaluzidwa wanga. Nyengo imeneyo, wandhu ambili yawo anikhulupilila siasiye kunikhulupilila, ni kung'anamukana ni kuipilana. Siachokele alosi ambili amthila, ni anyiiwo siwanyenge wandhu ambili.

Soma Matayo 24