AROMA 11:5-6
AROMA 11:5-6 BLPB2014
Choteronso nthawi yatsopano chilipo chotsalira monga mwa kusankha kwa chisomo. Koma ngati kuli ndi chisomo, sikulinso ndi ntchito ai; ndipo pakapanda kutero, chisomo sichikhalanso chisomo.
Choteronso nthawi yatsopano chilipo chotsalira monga mwa kusankha kwa chisomo. Koma ngati kuli ndi chisomo, sikulinso ndi ntchito ai; ndipo pakapanda kutero, chisomo sichikhalanso chisomo.