Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

MARKO 14:23-24

MARKO 14:23-24 BLPB2014

Ndipo anatenga chikho, ndipo pamene adayamika, anapereka kwa iwo; ndipo iwo onse anamweramo. Ndipo Iye anati kwa iwo, Ichi ndi mwazi wanga wa chipangano, wothiridwa chifukwa cha anthu ambiri.

Mipango ya Kusoma Bila Malipo na Ibada zinazohusiana na MARKO 14:23-24