HAGAI Mau Oyamba
Mau Oyamba
Mneneriyu adalalika mau ake chaka cha 520 BC., Ayuda ena atabwerera ku Yerusalemu kuchokera ku ukapolo. Anthuwo anali atabwerera ku ukapolo namakhala ku Yerusalemu kwa zaka zingapo, koma Kachisi anali bwinja lenileni. Atsogoleri anapereka uthenga kwa anthu kuti amangenso Kachisi, ndipo Ambuye akulonjeza kuti m'tsogolo anthu ake adzakhala pabwino ndi pa mtendere.
Za mkatimu
Yehova awalamula kuti amangenso Nyumba yake 1.1-15
Mau ena owalimbitsa mtima Ayudawo 2.1-23
Iliyochaguliwa sasa
HAGAI Mau Oyamba: BLPB2014
Kuonyesha
Shirikisha
Nakili
Je, ungependa vivutio vyako vihifadhiwe kwenye vifaa vyako vyote? Jisajili au ingia
The Bible in Chichewa Published as Buku Lopatulika
Bible Society of Malawi
HAGAI Mau Oyamba
Mau Oyamba
Mneneriyu adalalika mau ake chaka cha 520 BC., Ayuda ena atabwerera ku Yerusalemu kuchokera ku ukapolo. Anthuwo anali atabwerera ku ukapolo namakhala ku Yerusalemu kwa zaka zingapo, koma Kachisi anali bwinja lenileni. Atsogoleri anapereka uthenga kwa anthu kuti amangenso Kachisi, ndipo Ambuye akulonjeza kuti m'tsogolo anthu ake adzakhala pabwino ndi pa mtendere.
Za mkatimu
Yehova awalamula kuti amangenso Nyumba yake 1.1-15
Mau ena owalimbitsa mtima Ayudawo 2.1-23
Iliyochaguliwa sasa
:
Kuonyesha
Shirikisha
Nakili
Je, ungependa vivutio vyako vihifadhiwe kwenye vifaa vyako vyote? Jisajili au ingia
The Bible in Chichewa Published as Buku Lopatulika
Bible Society of Malawi