Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

AEFESO 3:20-21

AEFESO 3:20-21 BLPB2014

Ndipo kwa Iye amene angathe kuchita koposaposatu zonse zimene tizipempha, kapena tiziganiza, monga mwa mphamvu ya kuchita mwa ife, kwa Iye ukhale ulemerero mu Mpingo ndi mwa Khristu Yesu, kufikira mibadwo yonse ya nthawi za nthawi. Amen.

Mipango ya Kusoma Bila Malipo na Ibada zinazohusiana na AEFESO 3:20-21