Chapa ya Youversion
Ikoni ya Utafutaji

2 AKORINTO 1:6

2 AKORINTO 1:6 BLPB2014

Koma ngati tisautsidwa, kuli chifukwa cha chitonthozo ndi chipulumutso chanu; ngati titonthozedwa, kuli kwa chitonthozo chanu chimene chichititsa mwa kupirira kwa masautso omwewo amene ifenso timva.