1
Maluko 1:35
Nyanja
NTNYBL2025
Umawamawa siku lidachatila, Yesu wadapita kubwalo kwa mujhi, pamalo yapo padalibe wandhu, kumeneko wadampembha Mnungu.
Linganisha
Chunguza Maluko 1:35
2
Maluko 1:15
Wadakamba, “Nyengo ya Mnungu yakwana yolamulila wandhu. Lapani ni kukhulupilila Uthenga Wabwino.”
Chunguza Maluko 1:15
3
Maluko 1:10-11
Yesu yapo wadachuuka mmajhi, pamwepo wadaona kumwamba kwamasulidwa, ni Mzimu Woyela udamchikila ngati nghunda. Mvekelo wa Mnungu udaveka kuchokela kumwamba, niukamba, “Iwe nde mwana wanga uyo nikukonda, nikondelechedwa ni iwe.”
Chunguza Maluko 1:10-11
4
Maluko 1:8
Ine nikubatizani kwa majhi, nambho iye siwakubatizeni kwa Mzimu Woyela.”
Chunguza Maluko 1:8
5
Maluko 1:17-18
Yesu wadaakambila, “Nichateni, nane sinikuyaluzeni mukhale owapeleka wandhu kwa ine, ngati umo mmavuwila njhomba.” Pampajha adavisia vilepa vao nikumchata.
Chunguza Maluko 1:17-18
6
Maluko 1:22
Wandhu yawo adamvela mayaluzo yake, adazizwa ndande siwamayaluze ngati umo amayaluzila oyaluza athauko la Musa, nambho iye wamayaluza ngati mundhu wa ulamulilo.
Chunguza Maluko 1:22
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video