1
ZEKARIYA 13:9
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndi gawo lachitatulo ndidzalitengera kumoto, ndi kuwayenga ngati ayenga siliva, ndi kuwayesa monga ayesa golide; adzaitana dzina langa, ndipo ndidzawamvera; ndidzati, Awa ndi anthu anga; ndi iwo adzati, Yehova ndi Mulungu wanga.
Linganisha
Chunguza ZEKARIYA 13:9
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video