1
ZEKARIYA 1:3
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Chifukwa chake uziti nao, Atero Yehova wa makamu: Bwererani kudza kwa Ine, ati Yehova wa makamu, ndipo Ine ndidzabwerera kudza kwa inu, ati Yehova wa makamu.
Linganisha
Chunguza ZEKARIYA 1:3
2
ZEKARIYA 1:17
Fuulanso, ndi kuti, Atero Yehova wa makamu: Midzi yanga idzalemerera ndi kufalikiranso; ndipo Yehova adzasangalatsanso Ziyoni, nadzasankhamo Yerusalemu.
Chunguza ZEKARIYA 1:17
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video