1
Eksodo 29:45-46
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ndidzakhala pakati pa Aisraeli ndikukhala Mulungu wawo. Adzadziwa kuti ine ndine Mulungu wawo amene ndinawatulutsa mʼdziko la Igupto kuti ndikhale pakati pawo. Ine ndine Yehova, Mulungu wawo.”
Porównaj
Przeglądaj Eksodo 29:45-46