1
Eksodo 24:17-18
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ulemerero wa Yehova uja unkaoneka ngati malawi a moto pamwamba pa phirilo. Ndipo Mose analowa mʼmitambo nakwera phiri. Iye anakhala ku phiriko 40 usana ndi usiku.
Porównaj
Przeglądaj Eksodo 24:17-18
2
Eksodo 24:16
Ulemerero wa Yehova unakhala pa phiri la Sinai, ndipo mtambo unaphimba phirilo kwa masiku asanu ndi limodzi. Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri Yehova anayitana Mose kuchokera mu mtambowo.
Przeglądaj Eksodo 24:16
3
Eksodo 24:12
Yehova anati kwa Mose, “Bwera kwa ine ku phiri kuno, ndipo udikire konkuno. Ndidzakupatsa miyala imene ndalembapo malemba kuti ndiwaphunzitse.”
Przeglądaj Eksodo 24:12