Logo YouVersion
BibliaPlanyNagrania wideo
Pobierz aplikację
Wybór języka
Ikona wyszukiwania

Popularne wersety biblijne z Eksodo 23

1

Eksodo 23:25-26

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Muzipembedza Yehova Mulungu wanu ndipo adzakudalitsani ndi chakudya ndi madzi ndiponso ndidzachotsa nthenda pakati panu. Palibe mkazi amene adzapite padera kapena kukhala wosabereka mʼdziko mwanu. Ndidzakupatsani moyo wautali.

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 23:25-26

2

Eksodo 23:20

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Taona Ine ndikutuma mngelo wanga patsogolo panu kuti akutetezeni mʼnjiramo ndi kukakufikitsani ku malo amene ndakonza.

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 23:20

3

Eksodo 23:22

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ngati mudzamvera iyeyu ndi kuchita zonse zimene Ine ndikunena, Ine ndidzakhala mdani wa adani anu ndipo ndidzatsutsana ndi onse otsutsana nanu.

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 23:22

4

Eksodo 23:2-3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Usatsate gulu la anthu ndi kuchita choyipa. Pamene ukupereka umboni mʼbwalo lamilandu, usakhotetse mlandu chifukwa chofuna kukondweretsa anthu ambiri. Ndipo poweruza mlandu wa munthu wosauka usamukondere.

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 23:2-3

5

Eksodo 23:1

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Usafalitse mbiri yabodza. Usathandize munthu wolakwa pomuchitira umboni wonama.

Porównaj

Przeglądaj Eksodo 23:1

Bezpłatne plany czytania i rozważania na temat: Eksodo 23

Poprzedni rozdział
Następny rozdział
YouVersion

Zachęcanie i wzywanie cię do codziennego szukania bliskości z Bogiem.

Misja

O YouVersion

Praca

Wolontariat

Blog

Prasa

Przydatne linki

Pomoc

Wesprzyj

Przekłady Biblii

Biblie audio

Języki Biblii

Werset dnia


Cyfrowa misja

Life.Church
Polski

©2026 Life.Church / YouVersion

Polityka prywatnościRegulamin
Program ujawniania luk w zabezpieczeniach
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest