YouVersion logo
BibelLeseplanerVideoer
Få appen
Språkvelger
Søkeikon

Populære bibelvers fra LUKA 19

1

LUKA 19:10

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.

Sammenlign

Utforsk LUKA 19:10

2

LUKA 19:38

Buku Lopatulika

BLP-2018

nanena, Wolemekezeka Mfumuyo ikudza m'dzina la Ambuye; mtendere mu Mwamba, ndi ulemerero mu Mwambamwamba.

Sammenlign

Utforsk LUKA 19:38

3

LUKA 19:9

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yesu anati kwa iye, Lero chipulumutso chagwera nyumba iyi, popeza iyenso ndiye mwana wa Abrahamu.

Sammenlign

Utforsk LUKA 19:9

4

LUKA 19:5-6

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo m'mene anadza pamalopo Yesu anakweza maso nati kwa iye, Zakeyo, fulumira, nutsike; pakuti lero ndiyenera kukhala m'nyumba mwako. Ndipo anafulumira, natsika, namlandira Iye wokondwera.

Sammenlign

Utforsk LUKA 19:5-6

5

LUKA 19:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Zakeyo anaimirira nati kwa Ambuye, Taonani, Ambuye, gawo limodzi la zanga zonse zogawika pakati ndipatsa osauka; ndipo ngati ndalanda kanthu kwa munthu monyenga, ndimbwezera kanai.

Sammenlign

Utforsk LUKA 19:8

6

LUKA 19:39-40

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Afarisi ena a m'khamu la anthu anati kwa Iye, Mphunzitsi, dzudzulani ophunzira anu. Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula.

Sammenlign

Utforsk LUKA 19:39-40

Gratis leseplaner og andakter relatert til LUKA 19

Forrige kapittel
Neste kapittel
YouVersion

Oppmuntrer og utfordrer deg til å søke nærhet med Gud hver dag.

Tjeneste

Om

Karrierer

Frivillig

Blogg

Presse

Nyttige lenker

Hjelp

Gi

Bibeloversettelser

Lydbibler

Bibelspråk

Dagens bibelvers


En digital tjeneste av

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

PersonvernerklæringVilkår
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Hjem

Bibel

Leseplaner

Videoer