YouVersion лого
БиблиТѳлѳвлѳгѳѳнүүд Бичлэгүүд
Апп-ыг аваарай
Хэл сонгогч
Хайлтын дүрс

LUKA 24-ын алдартай Библийн эшлэлүүд

1

LUKA 24:49

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo onani, Ine nditumiza pa inu lonjezano la Atate wanga; koma khalani inu m'mudzi muno, kufikira mwavekedwa ndi mphamvu yochokera Kumwamba.

Харьцуулах

LUKA 24:49 г судлах

2

LUKA 24:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Palibe kuno Iye, komatu anauka; kumbukirani muja adalankhula nanu, pamene analinso m'Galileya

Харьцуулах

LUKA 24:6 г судлах

3

LUKA 24:31-32

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo maso ao anatseguka, ndipo anamzindikira Iye; ndipo anawakanganukira Iye, nawachokera. Ndipo anati wina kwa mnzake, Mtima wathu sunali wotentha m'kati mwathu nanga m'mene analankhula nafe m'njira, m'mene anatitsegulira malembo?

Харьцуулах

LUKA 24:31-32 г судлах

4

LUKA 24:46-47

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo anati kwa iwo, Kotero kwalembedwa, kuti Khristu amve zowawa, nauke kwa akufa tsiku lachitatu; ndi kuti kulalikidwe m'dzina lake kulapa ndi kukhululukidwa kwa machimo kwa mitundu yonse, kuyambira ku Yerusalemu.

Харьцуулах

LUKA 24:46-47 г судлах

5

LUKA 24:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda. Ndipo m'mene analowa sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Харьцуулах

LUKA 24:2-3 г судлах

Өмнөх Бүлэг
Дараагийн Бүлэг
YouVersion

Таныг өдөр бүр Бурхантай дотно харилцаа тогтоохыг урамшуулж, уриалж байна.

Үйлчлэл

Тухай

Ажил мэргэжил

Сайн дурын ажилтан

Блог

Хэвлэл мэдээлэл

Хэрэгтэй холбоосууд

Тусламж

Хандивлах

Библийн орчуулгууд

Аудио Библи

Библийн хэлүүд

Ѳнѳѳдрийн эшлэл


Дижитал үйлчлэл

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion-ы

Нууцлалын бодлогоНөхцөл
Эмзэг байдлыг тодруулах хөтөлбөр
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Нүүр хуудас

Библи

Тѳлѳвлѳгѳѳнүүд

Бичлэгүүд