1
MARKO 3:35
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pakuti aliyense achita chifuniro cha Mulungu, yemweyo ndiye mbale wanga, ndi mlongo, ndi amai.
താരതമ്യം
MARKO 3:35 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MARKO 3:28-29
Indetu, ndinena ndi inu, Adzakhululukidwa machimo onse a ana a anthu, ndi zamwano zilizonse adzachita mwano nazo; koma aliyense adzachitira Mzimu Woyera mwano alibe kukhululukidwa nthawi yonse, koma anapalamuladi tchimo losatha
MARKO 3:28-29 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MARKO 3:24-25
Ndipo ufumu ukagawanika pa uwu wokha, sukhoza kukhazikika. Ndipo nyumba ikagawanika pa iyo yokha, sikhoza kukhazikika nyumbayo
MARKO 3:24-25 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MARKO 3:11
Ndipo mizimu yonyansa, m'mene inamuona Iye, inamgwadira, nifuula, niti, Inu ndinu Mwana wa Mulungu.
MARKO 3:11 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ