1
MARKO 4:39-40
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo anauka, nadzudzula mphepo, nati kwa nyanja, kuti, Tonthola, khala bata. Ndipo mphepo inaleka, ndipo kunagwa bata lalikulu. Ndipo ananena nao, Muchitiranji mantha? Kufikira tsopano mulibe chikhulupiriro kodi?
താരതമ്യം
MARKO 4:39-40 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MARKO 4:41
Ndipo iwo anachita mantha akulu, nanenana wina ndi mnzake, Uyu ndani nanga, kuti ingakhale mphepo ndi nyanja zimvera Iye?
MARKO 4:41 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MARKO 4:38
Ndipo Iye mwini anali kutsigiro, nagona tulo pamtsamiro; ndipo anamuutsa Iye nanena kwa Iye, Mphunzitsi, kodi simusamala kuti titayika ife?
MARKO 4:38 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MARKO 4:24
Ndipo ananena nao, Yang'anirani chimene mukumva; ndi muyeso umene muyesera nao udzayesedwa kwa inu; ndipo kudzaonjezedwa kwa inu.
MARKO 4:24 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MARKO 4:26-27
Ndipo ananena, Ufumu wa Mulungu uli wotero, monga ngati munthu akataya mbeu panthaka; nakagona ndi kuuka, usiku ndi usana, ndipo mbeu zikamera, ndi kukula, iye sadziwa umo zichitira.
MARKO 4:26-27 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MARKO 4:23
Ngati munthu ali nao makutu akumva, amve.
MARKO 4:23 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ